30/05/2024
MKANGANO WA UKULU(The Great Controversy)
Kotale uyuyu...mmmmm muli minofu abare
🏃🏃🏃🏃
JESUS IS COMING SOON
30/05/2024
MKANGANO WA UKULU(The Great Controversy)
Kotale uyuyu...mmmmm muli minofu abare
🏃🏃🏃🏃
10/04/2023
CHIBVU 3:9
Taona,ndikupatsa ena oturuka m'sunagoge wa satana akudzinenera okha ali Ayuda,osakhala Ayuda,komatu anama;taona ,ndidzawadzetsa alambire pa mapazi ako,nazindikire kt ine ndakukonda,
Alipo ena amazitcha akhristu asali akhristu,kuziyenereza pa maso pa a anthu ngati opemphera,otumikira,ma prophet,abusa km pa maso pa Mulungu ali osakwanira,tikuyenera zi ntchito zathu zikhale zofanana monga ife otumikira ake..Amen.
03/04/2023
Iyi ndiye link ya group yi pa wtsp or +27738756109,Amen.
📖Evangelist.Ronald Lamba📖 WhatsApp Group Invite
08/01/2023
OWERENGA KHALA MASO
20/12/2022
Kutengera ndi momwe ndimalimvera Bible maka pa Exodus 20:4,5..ndidapeza kt Yehova Mulungu,mwana komanso mzimu oyera mu utatu mu umwini wake,sitikuyenera kumamupembeza kudzera mu zojambura,ziboliboli km kudzera mu mau bc,inunso mumamva momwemo,nanga cfkwa ciani muli ndi ziboliboli ma nyumba,ma office,ma church,mu khosi mwanu,mu galimoto yanu,zofananiza Mu Umulungu utatu ngati mukuzilambira ndi kuzikhulupilira ngati Yehova Mulungu,Mwana ngakhalenso mzimu oyera,kd mukatero simumakhala mukulambira Fano?
09/11/2022
Moni ana a Mulungu konse komwe tili?
09/11/2022
Moni ana apa ulendo?
11/10/2022
Marko 16:16
Kd mau oti "UBATIZO"amatanthauzanji,nanga inu muli ndi kuonjerapo motani pa zomwe mumaziziwa pa mau amewa?.
YOBU 2:10, kt tilimvetse ofunika kuyambira pa mdime 1 ya chapter cimeneci ca Yobu 2, inu mwaphunzirapo zotani?
Pangani like page yanga, kt mudalitsike ndi mau a Muliko kudzera mu buku lake lotchedwa BAIBULO, kulimbikisana za cisautso cikudzaci, mdzukiro, kuziwa za mu nthawi yomwe tili potengera (Daniel chapter 2 komanso Revelation 14:6) ndi Jerusalem watsopano.Tiyeni tikhale limodzi, musandisiye ndekha, Amen!!