Malawi Islamic Arts

Malawi Islamic Arts

Share

Malawi Islamic Arts is a Non-Profit Organization that Uses various platforms to inspire and educate both Muslim and Non-Muslims.

Our Goal is To provide a platform for Muslims and promote local Islamic talent through recognition and accessibility. Malawi Islamic Arts have a Website that provides online Islamic Arts and information due to lack of resourceful Online platforms for . The platform is set to promote online quality services and also to improve islamic information desermination standards among Muslims. The init

15/04/2026

*MALAWI ISLAMIC ARTS*

Malawi Islamic Arts ndi tsamba lomwe limathandiza Achinyamata aluso kuti afikile anthu ochuluka mukamphindi kochepa ndipo ndi tsamba lokhalo la pa internet lomwe lili ngati nkhokwe yopezela mitsangalutso yosiyana siyana komanso Zina zokhudza Chikhululupiliro Cha Chisilamu.

Monga mukudziwa tsambali limapezeka ndi zinthu Monga:

- Ma Ulaliki (Bayan)
- Quran (yotanthauzila muchichewa komaso Chizungu
- Ndakatulo
- Ma Nasheed

ndizina zambili.

Pakufuna kupitiliza ndi zintchito zimenezi komaso Kuthandiza Achinyamata aluso muno MMalawi, tsopano pa tsambali Achinyamata Aluso atha Kutsekula account yomwe iziwapatsa mwayi opanga:

1. Kuika zinthu pa Internet (Mwaokha
2. Kugulitsa komaso kukhazikitsa mitengo ya Ma luso awo
3. Kuona momwe Maluso awo akuchitila patsambali monga kuona chiwelengelo Cha ovela, Ogula komaso omwe apanga download Maluso awo.
4. Kutha kulumikizitsa zinthu zawo ndi tsamba la *YouTube* kuti zisavute kagawidwe.

Zakhale nafe Limodzi pa Mkumano wapa Internet omwe tizakhale tikuonetsa kaonekedwe Ka tsopano Ka website komanso Kuphunzitsa kapangidwe upload kazinthu zanu.

Tsikundi pa *25 April* kudzera pa *Google Meet.*

Kuti mudziwe zambili tipeze pa
WhatsApp: +265 998 737 873

Malawi Islamic Arts
Provision of dhikr through Arts

15/04/2026

Website yanyuwani pa 25 Epulo pano

Zomwe website yanyuwani idzichita

*kupanga upload nokha ma nsheed anu ndi ndakatulo komanso ma video
*kugulitsa luso lanu (nasheed,ndakatulo, ma video) pa mtengo okhumba kumtima kwanu

Tiyeni pa 25 April nthawi ya 8koloko madzulo ma artist tiphunzile mmene tingapangile upload komanso kugulitsa luso lathu

Link to join WhatsApp group

https://chat.whatsapp.com/FL42ZHymouiKcSC1qJS6bf?mode=gi_t

09/03/2026

Ulaliki wa mitala nde Mweeetu!!! Mano onse 40 panja.
Koma akati abaya 210 pin kuipitsa Nkhope ngati akumetani.

20/02/2026
13/02/2026

1. Solomon ...... 700 wives + 300 concubines
2. Rehoboam ...... 18 wives + 60 concubines
3. Abijah ...... 14 wives + concubines
4. David ...... 8 wives + multiple concubines
5. Jacob ...... 4 wives
6. Esau …..... 3 wives
7. Abraham...... 2 wives + 1 concubine
8. Elkanah …..... 2 wives
9. Lamech ...... 2 wives

Kumawelenga Baibulo mwanzeru👀

Polygamist men were literally the foundation of the Bible and they all found favor in the eyes of God.

Abraham, Jacob, David & Solomon - The Bible’s Polygamy Stories They Don’t Tell You.

Enewe good night🤓

08/02/2026

Tili mu mwezi wa ma Nikkah a Fast Fast!!

Photos from Malawi Islamic Arts's post 07/02/2026

Ramadhan Dos and Donts

02/02/2026

Mafayilo atsopano omwe atulutsidwa okhudza Epstein waku america akuonetsa ma email omwe akufotokoza za kutumizidwa kwa nsalu yopatulika yochokera ku Kaaba ku Makkah, nsalu zi zinaperekedwa ndi ku gulitsidwa kwa Jeffrey Epstein, yemwe ndi olemera kwambiri komanso anali ndi mulandu wo gwiririra.

Maimelo amenewa, olembedwa mu February ndi March 2017, akusonyeza mayi wa bizines dzina lake Aziza Al-Ahmadi ankagwira ntchito ndi Abdullah Al-Maari zokhudzana kumugukitsa epstein nsalu yakuda yokongoletsedwa ndi golide yomwe imaphimba Kaaba, malo opatulika kwambiri mu Chisilamu ku Saudi Arabia.

01/02/2026

Ma muslim sisters oyika ma nails inu,

Nde mwati Istinja mmapanga bwanji??

😂😂😂😂😂😂😂😂😂

30/01/2026

iiii zinthu zake 🥱🥱🥱

30/01/2026

Every Muslim parent should teach their children this five things 👇

1. Tawheed
teach them to know Allah, love Him, and rely on Him.
"Whoever Allah guide, none can misguide him."
Quran 39:37)

2. Ṣalāh
Make prayer a habit before it becomes an obligation.
“Command your family to pray and be steadfast in it.” (Qur’an 20:132)

3. Good Character (Akhlaq)
Manners before knowledge. Kind words, honesty, mercy.
“The best of you are those with the best character.” (Hadith – Tirmidhi)

4. Halāl & Ḥarām Awareness
Teach them what pleases Allah and what displeases Him.
“O my son, even if a deed is the weight of a mustard seed…” (Qur’an 31:16)

5. Love for the Qur’an & Sunnah
Let the Qur’an be their companion, not just a book.
“The best of you are those who learn the Qur’an and teach it.” (Bukhari)

Reminder for parents:
Children learn more from what we do than what we say.

O Allah, rectify our offspring and make them the comfort of our eyes. Āmīn

Sister Saratu Yahaya

12/01/2026

Chete kuyang’anira kumanga mzikiti

Want your school to be the top-listed School/college in Blantyre?

Click here to claim your Sponsored Listing.

Location

Telephone

Address


Blantyre
265