Voice of prophecy Bible School in Chichewa

Voice of prophecy Bible School in Chichewa

Share

To provide Bible trueth through Bible trueth and teachings.

01/05/2025

Pa vesi 115 paja akutionesa zomwe zimatilepheresa kuti kuunika kwa panjira zathu ndi kukhala nyali zomwe mafuta alimo okwanira kufikira kudza kwa Mkwati adzifotokoza bwino ndithu

01/05/2025

Buku loposa mabuku onseli limamuunikira munthu wina aliyense mmene angayendere mokhulupirika komanso njira zake zonse zimakhala zoongoka zokha zokha

01/05/2025

105Mau anu ndiwo nyali ya ku mapazi anga,

Ndi kuunika kwa panjira panga,

01/05/2025

Tiyeni timve pa Masalmo 119:105

01/05/2025

Buku lolimeneli ndilimene lili ndi malamulo a Yehova

01/05/2025

115Mundicokere ocita zoipa inu;

Kuti ndisunge malamulo a Mulungu wanga.

01/05/2025

Werengani Masalimo 119:115

01/05/2025

Kodi buku loposa mabuku onse ndi litilo?

29/04/2025

Katundu wanu wa ucimo mumusezese Yesu Khristu kuti alunyamulireni zothodwetsa zanu. Pakuti anati " ldzani kwa lne nonse olema ndi othodwa ndipo ndidzakutulani akatundu anu, senzani goli langa popeza lili lopepuka"

29/04/2025

Yesu Khristu anati ' lne ndine njira, coonadi ndi moyo.Okhulupirira lne angakhale amwalira adzakhala nao moyo osatha.' Kodi iwe ukhulupirira zimenezi ?!

23/04/2025

Yohane 7 vesi ya 32

23/04/2025

Tiyamba kuphunzira maphunziro athu akupeza kuyambira pa 1 May, 2025 . Cotero dziwani kuti muli olandiridwa ku sukulu imeneyi

Want your school to be the top-listed School/college in Blantyre?

Click here to claim your Sponsored Listing.

Location

Category

Telephone

Address


Mugabe
Blantyre