Pa vesi 115 paja akutionesa zomwe zimatilepheresa kuti kuunika kwa panjira zathu ndi kukhala nyali zomwe mafuta alimo okwanira kufikira kudza kwa Mkwati adzifotokoza bwino ndithu
Voice of prophecy Bible School in Chichewa
To provide Bible trueth through Bible trueth and teachings.
Buku loposa mabuku onseli limamuunikira munthu wina aliyense mmene angayendere mokhulupirika komanso njira zake zonse zimakhala zoongoka zokha zokha
105Mau anu ndiwo nyali ya ku mapazi anga,
Ndi kuunika kwa panjira panga,
Tiyeni timve pa Masalmo 119:105
Buku lolimeneli ndilimene lili ndi malamulo a Yehova
115Mundicokere ocita zoipa inu;
Kuti ndisunge malamulo a Mulungu wanga.
Werengani Masalimo 119:115
Kodi buku loposa mabuku onse ndi litilo?
Katundu wanu wa ucimo mumusezese Yesu Khristu kuti alunyamulireni zothodwetsa zanu. Pakuti anati " ldzani kwa lne nonse olema ndi othodwa ndipo ndidzakutulani akatundu anu, senzani goli langa popeza lili lopepuka"
Yesu Khristu anati ' lne ndine njira, coonadi ndi moyo.Okhulupirira lne angakhale amwalira adzakhala nao moyo osatha.' Kodi iwe ukhulupirira zimenezi ?!
Yohane 7 vesi ya 32
Tiyamba kuphunzira maphunziro athu akupeza kuyambira pa 1 May, 2025 . Cotero dziwani kuti muli olandiridwa ku sukulu imeneyi
Click here to claim your Sponsored Listing.
Location
Category
Contact the school
Telephone
Website
Address
Mugabe
Blantyre