The Hans Wehr

The Hans Wehr

Share

Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from The Hans Wehr, Education Website, Zomba.

02/04/2026

الدنيا جيفة ، والأسد لا يقع على الجِيَف

Dziko lapansi ndi zovunda, ndipo mkango sudya nyama,” ndi mwambi wofala umene umasonyeza maganizo kapena nzeru inayake. Mwachidule, mwambiwu umatanthauza kuti: - “Dziko ndi zovunda” likutanthauza kuti dziko lapansi langopita pang’onopang’ono ndipo ladzala ndi mavuto, katangale, ndi kupanda chilungamo. - "Mkango sudya nyama zovunda" zikutanthauza kuti munthu wolemekezeka, wamphamvu, kapena wolimba mtima sagwadira kapena kudzichotsera ulemu ndi zinthu zopanda pake kapena zachinyengo. Chifukwa chake, mwambiwu ukuwonetsa kuti munthu wolemekezeka kapena wamphamvu sagonja kapena kutsika ku zoyipa, ngakhale kuti dziko lapansi lili ndi zovuta kapena zovuta.

The Hans Wehr Education website

18/03/2026

Capital city ya Saudi Arabia (Riyadh) ikuyaka Moto

18/03/2026

Mamuna mnzako mpachulu

Team Iran let's gather here

FOLLOW Hans Wehr

18/03/2026

Mwezi sudaoneke

23/02/2026

Assalamu alaykum warahmatullah wabarakaatuh

Mwadzuka bwanj kulikonse komwe muli?

Kaya Swaum wanu akuyenda bwanji?

02/02/2026

Assalamu alaykum warahmatullah wabarakaatuh

18/01/2026

Dua podzuka
الحمدلله الذي أحيانا بعد ما أماتنا وإليه النشور

17/01/2026

Ngati tadzuka ndi moyo tiyeni timuyamike Mulungu

15/12/2025

Muhadith imene adailandira Abi hurairah, Allah atsangalale naye, iye adat adanena mtumiki wa Mulungu mtendere ndi Madalitso apite Kwa iye.Anthu 7 adzakhala pansi panthuzi wa Mulungu tsiku lachiweruzo,tsiku lomwe sikudzakhala nthuzi winauliwonse kupatula nthuzi wa Mulungu ndipo nthuzi umenewo udzakhala pansi pampando wake wachifumu.

1.Munthu oyamba ndi Mtsogoleri wa chilungamo.Kwa amene Allah watipatsa utsogoleri tiyeni tiugwiritsire ntchito mwachilungamo tisawapondereze anthu ena lero lino Deen yathu yalowa pansi chifukwa chakupondereza.

Munthu Wachiwiri ndi Mnyamata amene adakula iyeyo akumupembedza Allah ndikukula iyeyo Ali muchimenecho kapena kumwalira iyey akumupembedzabe Allah ndiye kuti patsiku lachiweruzo akakhala pansi pa nthuzi wa Allah.

Kwa lero tilekezere p***a

Osaiwala like and share

15/12/2025

Tiyen tipewe kuchita zinthu zimene zingaonoke Moyo wathu

15/12/2025

Assalamu alaykum warahmatullah wabarakaatuh

Mwadzuka bwanj kulikonse komwe muli

15/12/2025
Want your school to be the top-listed School/college in Zomba?

Click here to claim your Sponsored Listing.

Location

Website

Address

Zomba