02/04/2026
الدنيا جيفة ، والأسد لا يقع على الجِيَف
Dziko lapansi ndi zovunda, ndipo mkango sudya nyama,” ndi mwambi wofala umene umasonyeza maganizo kapena nzeru inayake. Mwachidule, mwambiwu umatanthauza kuti: - “Dziko ndi zovunda” likutanthauza kuti dziko lapansi langopita pang’onopang’ono ndipo ladzala ndi mavuto, katangale, ndi kupanda chilungamo. - "Mkango sudya nyama zovunda" zikutanthauza kuti munthu wolemekezeka, wamphamvu, kapena wolimba mtima sagwadira kapena kudzichotsera ulemu ndi zinthu zopanda pake kapena zachinyengo. Chifukwa chake, mwambiwu ukuwonetsa kuti munthu wolemekezeka kapena wamphamvu sagonja kapena kutsika ku zoyipa, ngakhale kuti dziko lapansi lili ndi zovuta kapena zovuta.
The Hans Wehr
Education website
18/03/2026
Capital city ya Saudi Arabia (Riyadh) ikuyaka Moto
18/03/2026
Mamuna mnzako mpachulu
Team Iran let's gather here
FOLLOW Hans Wehr
23/02/2026
Assalamu alaykum warahmatullah wabarakaatuh
Mwadzuka bwanj kulikonse komwe muli?
Kaya Swaum wanu akuyenda bwanji?
02/02/2026
Assalamu alaykum warahmatullah wabarakaatuh
18/01/2026
Dua podzuka
الحمدلله الذي أحيانا بعد ما أماتنا وإليه النشور
17/01/2026
Ngati tadzuka ndi moyo tiyeni timuyamike Mulungu
15/12/2025
Muhadith imene adailandira Abi hurairah, Allah atsangalale naye, iye adat adanena mtumiki wa Mulungu mtendere ndi Madalitso apite Kwa iye.Anthu 7 adzakhala pansi panthuzi wa Mulungu tsiku lachiweruzo,tsiku lomwe sikudzakhala nthuzi winauliwonse kupatula nthuzi wa Mulungu ndipo nthuzi umenewo udzakhala pansi pampando wake wachifumu.
1.Munthu oyamba ndi Mtsogoleri wa chilungamo.Kwa amene Allah watipatsa utsogoleri tiyeni tiugwiritsire ntchito mwachilungamo tisawapondereze anthu ena lero lino Deen yathu yalowa pansi chifukwa chakupondereza.
Munthu Wachiwiri ndi Mnyamata amene adakula iyeyo akumupembedza Allah ndikukula iyeyo Ali muchimenecho kapena kumwalira iyey akumupembedzabe Allah ndiye kuti patsiku lachiweruzo akakhala pansi pa nthuzi wa Allah.
Kwa lero tilekezere p***a
Osaiwala like and share
15/12/2025
Tiyen tipewe kuchita zinthu zimene zingaonoke Moyo wathu
15/12/2025
Assalamu alaykum warahmatullah wabarakaatuh
Mwadzuka bwanj kulikonse komwe muli