Bismillah Rahman Rahim
AlGaffar =The forgiving
Frequently recited Allah will remove Love of the world from his heart, and will have a good death.
M'dzina la Allah wachifundo komanso chisoni chambiri.
AlGaffar= Okhuluruka
Kutchula pafupi pafupi dzina limeneli Allah adzamuchotsera Munthu kukonda za mdziko ndipo azapanga imfa yake kukhala yofewa.
Machilitso M'chisilamu
Answer the questions that will be asked here and stand a chance of winning Airtime
Kod mumadziwa k*t dzina limeneli ndi lalikulu kwambiri?
Munthu amene angatchule dzina limeneli mobwerezabwereza ka 1000 ,
Mulungu adzayeretsa mtima wake kuchokera ku zoipa.
Komanso munthu amachira ku mnthenda yosachizika. Akuyenera k*tchula mnthenda imene akudwala ndikupempha kwa
Mulungu ndipo mwachifuniro cha Mulungu iye adzachila
Those who answered correctly their names Will be mentioned here.
The lucky winners of last week's question will receive their reward in this week.
Inshallah
Today's question
What does the word Quran mean?
Funso lathu la lero
Kodi mau ok*ti Quran amatanthauza Chan?
Remember: if you answered correctly you may have a chance of winning airtime
+265 only🇲🇼
Invite your friends to like this page
To reach 100likes.
And soon we are going to asking questions so that you may stand a chance of winning airtime
Tomorrow we're going to start asking questions..
Invite your friends to like our page and you will be among the 5 lucky winners of airtime
Pangani like page iyi
Osati post
بسم الله الر ØÙ…Ù† الر ØÙŠÙ…
Lachisanu tiyamba kufunsa mafunso ..
Ndipo anthu 5 amwai azilandila airtime
Pangani like page iyi k*t muzilandira mafunso
Click here to claim your Sponsored Listing.